Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2018

Pulogalamu ya 2018 “Limbani Mtima.” Msonkhano Wachigawo wa Mboni za Yehova.

Lachisanu

Pulogalamu ya tsiku limeneli yachokera pa Yoswa 1:7—“Khala wolimba mtima kwambiri ndipo uchite zinthu mwamphamvu.”

Loweruka

Kodi tingatani kuti tizilankhula mawu a Mulungu mopanda mantha?

Lamlungu

Pali zinthu zina zomwe zichitike m’tsogolomu, ndipo anthu a Mulungu adzafunika kukhala olimba mtima.

Mawu kwa Osonkhana

Dziwani zoyenera kuchita pa msonkhano wachigawo.