‘Yesetsani Kufunafuna Yehova Kuti Mupitirize Kukhala ndi Moyo’
Kodi kufunafuna Yehova kumatanthauza chiyani?
-
Kumatanthauza kupitiriza kuphunzira za iye komanso kutsatira mfundo zake pa moyo wathu
Kodi chinkachitika n’chiyani Aisiraeli akasiya kufunafuna Yehova?
-
Ankasiya ‘kudana ndi zoipa ndipo sankakonda zabwino’
-
Ankayamba kuchita zinthu zongodzisangalatsa okha
-
Ankasiya kutsatira malamulo a Yehova
Kodi Yehova watipatsa zinthu ziti pofuna kutithandiza kuti tizimufunafuna?