Salimo 134:1-3

Nyimbo Yokwerera Kumzinda. 134  Tamandani Yehova,+Inu nonse atumiki a Yehova,+Inu amene mumaimirira m’nyumba ya Yehova usiku.+   Pamene mukupemphera mutakweza manja anu, muzikhala oyera,+Ndipo tamandani Yehova.+   Yehova, amene ndiye Wopanga kumwamba ndi dziko lapansi,+Akudalitseni ali ku Ziyoni.+

Mawu a M'munsi